Kodi mukudziwa kuti amene adafa Ali ndi Yesu akuposa amene Ali ndi moyo koma opanda Yesu? Taganizani anthu amuna okhaokha kumagonana kapena akazi okhaokha, zomwe olo Galu sangachite.
Inu amene mulibe Yesu mukudziwa koma kuti Ambuye amakukondani? Si uyu muli pantchito yabwino,mudaphu
nzira,muli pabanja,ndinu olemera. Bwanji mulape lero posiya zigololo,mitala,ufiti,kuba,kuchotsa mimba,kuledzera,kusuta,kusintha amuna/akazi ngati sapato?
Ndikukuitanani ine m’bale wanu kuti bwerani kwa Yesu lero kuti mupulumuke. Mateyu 11:28-30.